1Ndipo ine ndinati,
2inu amene mumadana ndi zabwino ndi kukonda zoyipa;
3inu amene mumadya anthu anga,
4Pamenepo adzalira kwa Yehova,
5Yehova akuti,
6Nʼchifukwa chake kudzakuderani,
7Alosi adzachita manyazi
8Koma kunena za ine, ndadzazidwa ndi mphamvu,
9Imvani izi, inu atsogoleri a nyumba ya Yakobo,
10inu amene mukumanga Ziyoni pokhetsa magazi,
11Atsogoleri ake amalandira chiphuphu kuti aweruze,
12Choncho chifukwa cha inu,