We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Mika 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Mika Mika 2 →

1Yehova anayankhula ndi Mika wa ku Moreseti pa nthawi ya ulamuliro wa Yotamu, Ahazi ndi Hezekiya, mafumu a ku Yuda. Awa ndi masomphenya amene iye anaona onena za Samariya ndi Yerusalemu.

2Tamverani, inu anthu a mitundu yonse,

3Taonani! Yehova akubwera kuchokera ku malo ake;

4Mapiri akusungunuka pansi pake,

5Zonsezi ndi chifukwa cha cholakwa cha Yakobo,

6“Choncho Ine ndidzasandutsa Samariya kukhala bwinja,

7Mafano ake onse ndidzawaphwanyaphwanya;

8Chifukwa cha zimenezi ine ndidzalira momvetsa chisoni;

9Pakuti chilonda cha Samariya nʼchosachizika;

10Musanene zimenezi ku Gati;

11Inu anthu okhala ku Safiro,

12Anthu amene amakhala ku Maroti akubuwula ndi ululu,

13Inu anthu okhala ku Lakisi

14Chifukwa chake perekani mphatso zolawirana

15Ndidzabweretsa mgonjetsi kudzalimbana ndi inu

16Metani mipala mitu yanu kuonetsa kuti mukulirira

Mika Mika 2 →