We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Maliro 4

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Maliro 3 Maliro Maliro 5 →

1Haa! Golide wathimbirira,

2Haa! Ana a Ziyoni amtengowapatali

3Ngakhale nkhandwe zimapereka bere

4Lilime la mwana lakangamira kukhosi

5Iwo amene kale ankadya zonona

6Kuyipa kwa anthu anga kunali kwakukulu

7Akalonga ake anali owala koposa chisanu chowundana

8Koma tsopano maonekedwe awo ndi akuda kuposa mwaye;

9Amene anaphedwa ndi lupanga aliko bwino kuposa

10Amayi achifundo afika

11Yehova wakwaniritsa ukali wake;

12Mafumu a pa dziko lapansi sanakhulupirire,

13Koma izi zinachitika chifukwa cha kuchimwa kwa aneneri ake

14Tsopano akungoyendayenda mʼmisewu ya mu mzinda

15Anthu akuwafuwulira kuti, “Chokani! Inu anthu odetsedwa!”

16Yehova mwini wake wawabalalitsa;

17Ndiponso maso athu atopa nʼkuyangʼana,

18Anthu ankalondola mapazi athu,

19Otilondola akuthamanga kwambiri

20Wodzozedwa wa Yehova, mpweya wathu wotipatsa moyo,

21Kondwera ndi kusangalala, mwana wamkazi wa Edomu.

22Iwe mwana wamkazi wa Ziyoni, chilango chako chidzatha;

← Maliro 3 Maliro Maliro 5 →