1Haa! Golide wathimbirira,
2Haa! Ana a Ziyoni amtengowapatali
3Ngakhale nkhandwe zimapereka bere
4Lilime la mwana lakangamira kukhosi
5Iwo amene kale ankadya zonona
6Kuyipa kwa anthu anga kunali kwakukulu
7Akalonga ake anali owala koposa chisanu chowundana
8Koma tsopano maonekedwe awo ndi akuda kuposa mwaye;
9Amene anaphedwa ndi lupanga aliko bwino kuposa
10Amayi achifundo afika
11Yehova wakwaniritsa ukali wake;
12Mafumu a pa dziko lapansi sanakhulupirire,
13Koma izi zinachitika chifukwa cha kuchimwa kwa aneneri ake
14Tsopano akungoyendayenda mʼmisewu ya mu mzinda
15Anthu akuwafuwulira kuti, “Chokani! Inu anthu odetsedwa!”
16Yehova mwini wake wawabalalitsa;
17Ndiponso maso athu atopa nʼkuyangʼana,
18Anthu ankalondola mapazi athu,
19Otilondola akuthamanga kwambiri
20Wodzozedwa wa Yehova, mpweya wathu wotipatsa moyo,
21Kondwera ndi kusangalala, mwana wamkazi wa Edomu.
22Iwe mwana wamkazi wa Ziyoni, chilango chako chidzatha;