We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Maliro 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Maliro 2 Maliro Maliro 4 →

1Ine ndine munthu amene ndaona masautso

2Wandipititsa kutali ndipo wandiyendetsa

3zoonadi anandikantha ndi dzanja lake

4Wakalambitsa khungu langa ndi mnofu wanga,

5Wandizinga ndi kundizungulira

6Wandikhazika mu mdima

7Wandimangira khoma kotero kuti sindingathawe,

8Ngakhale pamene ndifuwula kapena kupempha chithandizo,

9Wanditsekera njira yanga ndi miyala yosema;

10Wandidikirira ngati chimbalangondo,

11Wandikokera pambali ndi kundingʼambangʼamba,

12Wakoka uta wake

13Walasa mtima wanga

14Ndinakhala choseketsa cha anthu anga onse;

15Wandidyetsa zowawa

16Wathyola mano anga ndi miyala;

17Wandichotsera mtendere;

18Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka

19Kukumbukira masautso anga ndi kusowa pokhala,

20Ine ndikuzikumbukira bwino izi,

21Komabe ndimakumbukira zimenezi,

22Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu,

23Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse;

24Mu mtima mwanga ndimati, “Yehova ndiye zanga zonse;

25Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye,

26nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha

27Nʼkwabwino kuti munthu asenze goli

28Akhale chete pa yekha,

29Abise nkhope yake mʼfumbi

30Apereke tsaya lake kwa iye amene angamumenye,

31Chifukwa Ambuye satayiratu

32Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,

33Pakuti sabweretsa masautso mwadala,

34Kuphwanya ndi phazi

35kukaniza munthu ufulu wake

36kumana munthu chiweruzo cholungama—

37Kodi ndani angayankhule zinthu nʼkuchitika

38Kodi zovuta ndi zabwino sizituluka

39Kodi nʼchifukwa chiyani munthu aliyense wamoyo amadandaula

40Tiyeni tisanthule ndi kuyesa njira zathu,

41Tiyeni tikweze mitima yathu ndi manja athu

42“Ife tachimwa ndi kuwukira

43“Mwadzikuta ndi mkwiyo ndi kutilondola ndipo

44Mwadzikuta mu mtambo

45Mwatisandutsa zinyatsi ndi zinyalala

46“Adani anthu atitsekulira pakamwa.

47Ife tadzazidwa ndi mantha pakuti tagwa mʼdzenje,

48Misozi mʼmaso mwanga ikungoti mbwembwembwe

49Misozi idzatsika kosalekeza,

50mpaka Yehova ayangʼane pansi

51Mtima wanga ukupweteka poona zimenezi

52Akundisaka ngati mbalame,

53Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje

54madzi anamiza mutu wanga

55Ndinayitana dzina lanu Inu Yehova,

56Inu munamva kudandaula kwanga. “Mundimvere

57Munafika pafupi pamene ndinakuyitanani,

58Inu Ambuye munandiwombola ku mlandu wanga;

59Yehova, mwaona zoyipa zimene andichitira.

60Mwaona kuzama kwa kubwezera kwawo,

61Inu Yehova mwamva kunyoza kwawo,

62manongʼonongʼo a adani anga

63Tawaonani! Kaya ali pansi kapena kuyimirira,

64Inu Yehova, muwabwezere chowayenera,

65Phimbani mitima yawo,

66Muwalondole mwaukali ndipo

← Maliro 2 Maliro Maliro 4 →