1Ine ndine munthu amene ndaona masautso
2Wandipititsa kutali ndipo wandiyendetsa
3zoonadi anandikantha ndi dzanja lake
4Wakalambitsa khungu langa ndi mnofu wanga,
5Wandizinga ndi kundizungulira
6Wandikhazika mu mdima
7Wandimangira khoma kotero kuti sindingathawe,
8Ngakhale pamene ndifuwula kapena kupempha chithandizo,
9Wanditsekera njira yanga ndi miyala yosema;
10Wandidikirira ngati chimbalangondo,
11Wandikokera pambali ndi kundingʼambangʼamba,
12Wakoka uta wake
13Walasa mtima wanga
14Ndinakhala choseketsa cha anthu anga onse;
15Wandidyetsa zowawa
16Wathyola mano anga ndi miyala;
17Wandichotsera mtendere;
18Choncho ndikuti, “Ulemerero wanga wachoka
19Kukumbukira masautso anga ndi kusowa pokhala,
20Ine ndikuzikumbukira bwino izi,
21Komabe ndimakumbukira zimenezi,
22Ife sitinawonongekeretu chifukwa chikondi cha Yehova ndi chachikulu,
23Zimaoneka zatsopano mmawa uliwonse;
24Mu mtima mwanga ndimati, “Yehova ndiye zanga zonse;
25Yehova ndi wabwino kwa amene amayembekezera Iye,
26nʼkwabwino kudikira chipulumutso cha
27Nʼkwabwino kuti munthu asenze goli
28Akhale chete pa yekha,
29Abise nkhope yake mʼfumbi
30Apereke tsaya lake kwa iye amene angamumenye,
31Chifukwa Ambuye satayiratu
32Ngakhale amabweretsa zowawa, Iye adzawachitira chifundo,
33Pakuti sabweretsa masautso mwadala,
34Kuphwanya ndi phazi
35kukaniza munthu ufulu wake
36kumana munthu chiweruzo cholungama—
37Kodi ndani angayankhule zinthu nʼkuchitika
38Kodi zovuta ndi zabwino sizituluka
39Kodi nʼchifukwa chiyani munthu aliyense wamoyo amadandaula
40Tiyeni tisanthule ndi kuyesa njira zathu,
41Tiyeni tikweze mitima yathu ndi manja athu
42“Ife tachimwa ndi kuwukira
43“Mwadzikuta ndi mkwiyo ndi kutilondola ndipo
44Mwadzikuta mu mtambo
45Mwatisandutsa zinyatsi ndi zinyalala
46“Adani anthu atitsekulira pakamwa.
47Ife tadzazidwa ndi mantha pakuti tagwa mʼdzenje,
48Misozi mʼmaso mwanga ikungoti mbwembwembwe
49Misozi idzatsika kosalekeza,
50mpaka Yehova ayangʼane pansi
51Mtima wanga ukupweteka poona zimenezi
52Akundisaka ngati mbalame,
53Ayesa kundipha pondiponya mʼdzenje
54madzi anamiza mutu wanga
55Ndinayitana dzina lanu Inu Yehova,
56Inu munamva kudandaula kwanga. “Mundimvere
57Munafika pafupi pamene ndinakuyitanani,
58Inu Ambuye munandiwombola ku mlandu wanga;
59Yehova, mwaona zoyipa zimene andichitira.
60Mwaona kuzama kwa kubwezera kwawo,
61Inu Yehova mwamva kunyoza kwawo,
62manongʼonongʼo a adani anga
63Tawaonani! Kaya ali pansi kapena kuyimirira,
64Inu Yehova, muwabwezere chowayenera,
65Phimbani mitima yawo,
66Muwalondole mwaukali ndipo