1Haa, Ambuye waphimba mwana wamkazi wa Ziyoni
2Ambuye anawononga midzi yonse ya Yakobo mopanda chifundo;
3Atakwiya kwambiri, Ambuye anathyola
4Wakokera uta wake pa ife ngati ndife adani;
5Ambuye ali ngati mdani;
6Wagwetsa malo ake okhalamo ngati khumbi la mʼmunda;
7Ambuye wakana guwa lake la nsembe
8Yehova anatsimikiza kugwetsa
9Zipata za Yerusalemu zalowa pansi;
10Akuluakulu a mwana wamkazi wa Ziyoni
11Maso anga atopa ndi kulira,
12Anawo akufunsa amayi awo kuti,
13Ndinganene chiyani za iwe?
14Masomphenya a aneneri ako
15Onse oyenda mʼnjira yako
16Adani ako onse akutsekulira pakamwa ndi kukunyoza;
17Yehova wachita chimene anakonzeratu;
18Mitima ya anthu
19Dzuka, fuwula usiku,
20Inu Yehova, onani, ndipo ganizirani:
21Anyamata ndi okalamba aligone pamodzi
22Ngati momwe mumayitanira pa tsiku la phwando,