We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Maliro 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Maliro Maliro 2 →

1Haa! Mzinda uja wasiyidwa wokhawokha,

2Ukulira mowawidwa mtima usiku wonse,

3Yuda watengedwa ku ukapolo,

4Misewu yopita ku Ziyoni ikulira,

5Adani ake asanduka mabwana ake;

6Ulemerero wonse wa mwana wamkazi wa Ziyoni

7Pa masiku a masautso ndi kuzunzika kwake,

8Yerusalemu wachimwa kwambiri

9Uve wake umaonekera pa zovala zake;

10Adani amulanda

11Anthu ake onse akubuwula

12“Kodi zimenezi mukuziyesa zachabe, inu nonse mukudutsa?

13“Anatumiza moto kuchokera kumwamba,

14“Wazindikira machimo anga onse

15“Ambuye wakana

16“Chifukwa cha zimenezi ndikulira

17“Ziyoni wakweza manja ake,

18“Yehova ndi wolungama,

19“Ndinayitana abwenzi anga

20“Inu Yehova, onani mmene ine ndavutikira!

21“Anthu amva kubuwula kwanga,

22“Lolani kuti ntchito zawo zoyipa zifike pamaso panu;

Maliro Maliro 2 →