1Haa! Mzinda uja wasiyidwa wokhawokha,
2Ukulira mowawidwa mtima usiku wonse,
3Yuda watengedwa ku ukapolo,
4Misewu yopita ku Ziyoni ikulira,
5Adani ake asanduka mabwana ake;
6Ulemerero wonse wa mwana wamkazi wa Ziyoni
7Pa masiku a masautso ndi kuzunzika kwake,
8Yerusalemu wachimwa kwambiri
9Uve wake umaonekera pa zovala zake;
10Adani amulanda
11Anthu ake onse akubuwula
12“Kodi zimenezi mukuziyesa zachabe, inu nonse mukudutsa?
13“Anatumiza moto kuchokera kumwamba,
14“Wazindikira machimo anga onse
15“Ambuye wakana
16“Chifukwa cha zimenezi ndikulira
17“Ziyoni wakweza manja ake,
18“Yehova ndi wolungama,
19“Ndinayitana abwenzi anga
20“Inu Yehova, onani mmene ine ndavutikira!
21“Anthu amva kubuwula kwanga,
22“Lolani kuti ntchito zawo zoyipa zifike pamaso panu;