We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 37

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 36 Yobu Yobu 38 →

1“Mtima wanga ukulumphalumpha pa chimenechinso

2Tamverani! Tamverani kubangula kwa liwu lake,

3Iye amaponya chingʼaningʼani chake pansi pa thambo lonse

4Pambuyo pake kubangula kwake kumamveka.

5Liwu la Mulungu limabangula mʼnjira zambiri zodabwitsa

6Amalamula chisanu chowundana kuti, ‘Igwa pa dziko lapansi,’

7Kuti anthu onse amene anawalenga athe kuzindikira ntchito yake.

8Zirombo zimakabisala

9Mphepo yamkuntho imatuluka ku malo ake,

10Mpweya wa Mulungu umawunditsa madzi

11Iye amadzaza mitambo ndi madzi a mvula,

12Mulungu amayendetsa mitamboyo

13Iye amagwetsa mvula kuti alange anthu,

14“Abambo Yobu, tamvani izi;

15Kodi mukudziwa momwe Mulungu amayendetsera mitambo

16Kodi mukudziwa momwe Mulungu amayalira mitambo,

17Inu amene mʼzovala zanu mumatuluka thukuta

18kodi mungathe kuthandizana naye kutambasula thambo

19“Tiwuzeni ife zoti tikanene kwa Iye;

20Kodi nʼkofunika kumudziwitsa Mulungu kuti ndili naye mawu?

21Tsopano munthu sangathe kuyangʼana dzuwa,

22Kuwala kwake kumaonekera cha kumpoto;

23Wamphamvuzonse sitingathe kumufikira pafupi ndi wa mphamvu zoposa;

24Nʼchifukwa chake anthu amamuopa kwambiri,

← Yobu 36 Yobu Yobu 38 →