1Ndipo Elihu anapitirira kuyankhula nati:
2“Mundilole pangʼono pokha ndipo ndikuonetsani
3Nzeru zanga ndimazitenga kutali;
4Ndithudi mawu anga si abodza;
5“Mulungu ndi wamphamvu, koma sanyoza anthu;
6Salola oyipa kuti akhalebe ndi moyo
7Iye saleka kuyangʼanira anthu olungama;
8Koma ngati anthu amangidwa ndi unyolo,
9Iye amawafotokozera zomwe anachita,
10Mulungu amawatsekula makutu kuti amve malangizo ake
11Ngati iwo amumvera ndi kumutumikira,
12Koma ngati samvera,
13“Anthu osapembedza amasunga mkwiyo mu mtima mwawo;
14Amafa akanali achinyamata,
15Koma ovutika, Iye amawapulumutsa pa mavuto awo;
16“Iye akukukopani inu kuti muchoke mʼmasautso,
17Koma tsopano inu mwapezeka wopalamula chifukwa cha kuyipa kwanu;
18Muchenjere kuti wina asakukopeni ndi chuma;
19Kodi chuma chanu
20Musalakalake kuti usiku ubwere,
21Muchenjere kuti musatembenukire ku uchimo,
22“Taonani, Mulungu ndi wamkulu ndiponso ndi wamphamvu.
23Kodi ndani amene anamuwuzapo Mulungu zoti achite,
24Kumbukirani kutamanda ntchito zake
25Anthu onse amaziona ntchitozo;
26Ndithudi, Mulungu ndi wamkulu, sitimudziwa nʼpangʼono pomwe!
27“Mulungu ndiye amakweza timadontho tamadzi kuthambo,
28mitambo imagwetsa mvulayo
29Kodi ndani amene angadziwe momwe mitambo imayendera,
30Taonani momwe amawalitsira zingʼaningʼani pa malo ake onse,
31Umu ndi mmene Iye amalamulira mitundu ya anthu
32Amadzaza manja ake ndi zingʼaningʼani,
33Mabingu ake amalengeza za kubwera kwa mvula yamkuntho;