We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 14

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 13 Yobu Yobu 15 →

1“Munthu wobadwa mwa amayi

2Amaphuka ngati duwa ndipo kenaka amafota;

3Kodi munthu wotereyo nʼkumuyangʼanitsitsa?

4Ndani angatulutse chabwino mʼchoyipa?

5Masiku a munthu ndi odziwikiratu;

6Choncho Inu mumufulatire ndipo mumuleke apumule

7“Mtengo uli nacho chiyembekezo:

8Mizu yake ingathe kukalamba mʼnthaka

9koma pamene chinyontho chafika udzaphukira

10Koma munthu amafa nayikidwa mʼmanda,

11Monga madzi amaphwera mʼnyanja

12momwemonso munthu amagona ndipo sadzukanso;

13“Aa, Inu mukanangondibisa mʼmanda

14Munthu akafa, kodi adzakhalanso ndi moyo?

15Inu mudzandiyitane ndipo ndidzakuyankhani;

16Ndithudi pamenepo mudzayangʼana mayendedwe anga

17Zolakwa zanga zidzakulungidwa mʼthumba;

18“Koma monga phiri limakokolokera ndi kuswekasweka

19monganso madzi oyenda amaperesera miyala

20Inu mumamugonjetsa kamodzinʼkamodzi ndipo munthuyo nʼkutheratu;

21Ana ake akamalemekezedwa, iyeyo sazidziwa zimenezo;

22Iye amangomva zowawa za mʼthupi lake

← Yobu 13 Yobu Yobu 15 →