We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 13

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 12 Yobu Yobu 14 →

1“Ndaziona ndi maso anga zonsezi,

2Zimene inu mukudziwa, inenso ndimazidziwa;

3Koma ine ndikulakalaka nditayankhula ndi Wamphamvuzonse

4Koma inu mukundipaka mabodza;

5Achikhala munangokhala chete nonsenu!

6Tsopano imvani kudzikanira kwanga;

7Kodi inu mudzayankhula moyipa kuyankhulira Mulungu?

8Kodi mudzaonetsa kuti Iyeyo ngokondera?

9Mulungu atayangʼanitsitsa, inu nʼkukupezani wosalakwa?

10Ndithudi, Iye angathe kukudzudzulani

11Kodi ulemerero wake sungakuopseni?

12Mawu anu anzeru ali ngati miyambi yopanda tanthauzo;

13“Khalani chete ndipo ndilekeni ndiyankhule;

14Chifukwa chiyani ndikuyika moyo wanga pa chiswe

15Ngakhale Iye andiphe, komabe ndidzamukhulupirira;

16Zoonadi, ichi ndiye chidzakhala chipulumutso changa

17Mvetserani mosamala mawu anga;

18Pakuti tsopano ndawukonzekera mlandu wanga,

19Kodi alipo wina amene angatsutsane nane?

20“Inu Mulungu, ndipatseni zinthu ziwiri izi,

21Muchotse dzanja lanu pa ine,

22Tsono muyitane ndipo ndidzayankha,

23Kodi zolakwa zanga ndi zingati ndipo machimo anga ndi angati?

24Chifukwa chiyani mukundifulatira

25Kodi mudzazunza tsamba lowuluka ndi mphepo?

26Pakuti Inu mwalemba zinthu zowawa zonditsutsa nazo

27Inu mwamanga miyendo yanga ndi maunyolo.

28“Motero munthu amatha ngati chinthu chofumbwa,

← Yobu 12 Yobu Yobu 14 →