We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 12

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 11 Yobu Yobu 13 →

1Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2“Ndithudi inuyo ndinu anthu

3Koma inenso ndili nazo nzeru ngati inu;

4“Ndasanduka chinthu choseketsa kwa abwenzi anga,

5Anthu amene ali pabwino amanyoza anzawo amene ali pa tsoka.

6Nyumba za anthu achifwamba zimakhala pa mtendere,

7“Koma funsa nyama zakuthengo ndipo zidzakuphunzitsa,

8kapena uyankhule ndi dziko lapansi ndipo lidzakuphunzitsa,

9Kodi mwa zonsezi ndi chiti chimene sichidziwa

10Mʼmanja mwake ndi mʼmene muli moyo wa cholengedwa chilichonse,

11Kodi khutu sindiye limene limamva mawu

12Kodi nzeru sipezeka pakati pa anthu okalamba?

13“Kwa Mulungu ndiye kuli nzeru ndi mphamvu;

14Chimene Iye wapasula palibe angachimangenso.

15Iyeyo akamanga mvula dziko limawuma;

16Kwa Iye kuli mphamvu ndi kupambana;

17Iye amalanda aphungu nzeru zawo

18Iye amachotsa zingwe zimene mafumu anawamanga nazo

19Iye amasocheretsa ansembe atawalanda nzeru zawo

20Iye amakhalitsa chete aphungu odalirika

21Iye amanyoza anthu otchuka

22Iye amatulutsira poyera zinthu zozama za mu mdima

23Iye amakuza mitundu ya anthu ndipo amayiwononganso;

24Iye amalanda nzeru za atsogoleri a dziko lapansi;

25Iwo amafufuzafufuza njira mu mdima wopanda chowunikira;

← Yobu 11 Yobu Yobu 13 →