1Uthenga umene Yehova anayankhula ndi mneneri Yeremiya wonena za mzinda wa Babuloni ndi anthu ake ndi uwu:
2“Lengeza ndi kulalika pakati pa anthu a mitundu ina,
3Mtundu wa anthu wochokera kumpoto wadzathira nkhondo Babuloni
4“Masiku amenewo, nthawi imeneyo,”
5Adzafunsa njira ya ku Ziyoni
6“Anthu anga ali ngati nkhosa zotayika;
7Aliyense amene anawapeza anawawononga;
8“Thawaniko ku Babuloni;
9Taonani, ndidzaukitsa gulu lankhondo lamphamvu la mitundu ina
10Motero Ababuloni adzafunkhidwa;
11“Inu Ababuloni, munawononga anthu anga osankhika.
12Koma mzinda wanu udzachititsidwa manyazi kwambiri.
13Chifukwa cha mkwiyo wa Yehova Babuloni adzakhala wopanda anthu
14“Inu okoka uta,
15Mufuwulireni mbali zonse pakuti wagonja.
16Chotsani ku Babuloni munthu wofesa mbewu aliyense,
17“Aisraeli ali ngati nkhosa zomwe zabalalika
18Nʼchifukwa chake Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti,
19Koma ndidzabwezera Israeli ku msipu wake
20Masiku amenewo, nthawi imeneyo,”
21“Lithireni nkhondo dziko la Merataimu
22Mʼdziko muli phokoso la nkhondo,
23Taonani mʼmene waphwanyikira ndi kuwonongekera
24Ndinakutchera msampha, iwe Babuloni,
25Yehova watsekula nyumba ya zida zake
26Mumenyane naye Babuloni mbali zonse.
27Iphani ankhondo ake onse.
28Tikumva anthu othawa nkhondo ochokera ku Babuloni
29“Itanani anthu oponya mivi kudzathira nkhondo Babuloni.
30Nʼchifukwa chake, anyamata ake adzaphedwa mʼmabwalo ake;
31“Taona, ndikukuthira nkhondo, iwe wodzikuzawe,”
32Wodzikuzawe udzapunthwa nʼkugwa
33Yehova Wamphamvuzonse akuti,
34Koma Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu;
35Yehova akuti,
36Imfa yalunjika pa aneneri abodza
37Imfa ilunjike pa akavalo ake ndi magaleta ake.
38Chilala chilunjike pa madzi ake
39“Nʼchifukwa chake nyama zakuthengo ndi afisi zidzakhala kumeneko
40Monga momwe Mulungu anawonongera Sodomu ndi Gomora
41“Taonani! Gulu lankhondo likubwera kuchokera kumpoto;
42Atenga mauta ndi mikondo;
43Mfumu ya ku Babuloni yamva za mbiri yawo,
44Taonani, monga mkango wochokera ku nkhalango ya ku Yorodani
45Nʼchifukwa chake imvani.
46Akadzagwa Babuloni padzakhala mfuwu waukulu ndipo dziko lapansi lidzanjenjemera,