We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yeremiya 49

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yeremiya 48 Yeremiya Yeremiya 50 →

1Yehova ananena izi:

2Koma nthawi ikubwera,”

3“Lirani, inu anthu a ku Hesiboni chifukwa wowononga uja wafika!

4Chifukwa chiyani mukunyadira

5Ndidzabweretsa zoopsa pa iwe

6“Komabe pambuyo pake, ndidzabwezera kwawo Aamoni,”

7Yehova Wamphamvuzonse ananena izi za Edomu:

8Inu anthu a ku Dedani, thawani,

9Kodi anthu othyola mphesa akanafika kwa inu

10Koma ine ndazivula zidzukulu za Esau.

11‘Siyani ana anu amasiye; Ine ndidzawateteza.

12Yehova akuti, “Ngati iwo amene sanali oyenera kulangidwa adzamwa chikho cha chiweruzo, ndiye muyesa kuti inuyo simudzalangidwa? Ayi ndithu simudzakhala osalangidwa. Mudzamwa ndithu chikhocho.

13Ine ndikulumbira, akutero Yehova, kuti mzinda wa Bozira udzasanduka bwinja, chinthu chochititsa mantha, chomachiseka ndiponso chotembereredwa. Mizinda yake yonse idzakhala mabwinja mpaka muyaya.”

14Ndamva uthenga wochokera kwa Yehova:

15“Ndidzakuchepetsani pakati pa anthu a mitundu ina.

16Kuopseza kwako kwakunyenga;

17“Dziko la Edomu lidzasanduka chinthu chochititsa mantha.

18Monga momwe anawonongekera Sodomu ndi Gomora,

19“Monga mkango wotuluka ku nkhalango za ku Yorodani

20Nʼchifukwa chake imvani. Izi ndi zimene Ine Yehova

21Akadzagwa Edomu padzakhala mfuwu waukulu ndipo dziko lapansi lidzanjenjemera;

22Taonani, mtundu wina udzachita kuwuluka

23Mawu a Yehova onena za Damasiko ndi awa:

24Anthu a ku Damasiko alefuka.

25Mzinda wotchuka

26Nʼchifukwa chake anyamata ake adzagwa mʼmisewu ndi kufa;

27“Ndidzatentha malinga a Damasiko;

28Mawu a Yehova onena za Kedara ndi maufumu a ku Hazori, amene Nebukadinezara mfumu ya Babuloni anawagonjetsa ndi awa:

29Landani matenti awo ndi nkhosa zawo,

30“Thawani mofulumira!

31“Nyamukani kathireni nkhondo mtundu wa anthu umene uli pamtendere,

32Ngamira zawo zidzafunkhidwa,

33“Hazori adzasanduka bwinja,

34Uthenga umene Yehova anapatsa mneneri Yeremiya wonena za Elamu, Zedekiya mfumu ya Yuda atangoyamba kulamulira ndi uwu:

35Yehova Wamphamvuzonse akuti,

36Ndidzabweretsa mphepo zinayi pa Elamu

37A ku Elamuwo ndidzachititsa mantha pamaso pa adani awo

38Ndidzakhazika mpando wanga waufumu ku Elamu

39“Komabe mʼtsogolomo ndidzabwezera

← Yeremiya 48 Yeremiya Yeremiya 50 →