1Ponena za Mowabu:
2Palibenso amene akutamanda Mowabu;
3Tamvani mfuwu wa anthu a ku Horonaimu.
4Mowabu wawonongeka;
5Anthu akukwera chikweza cha ku Luhiti,
6Thawani! Dzipulumutseni;
7Popeza inu munkadalira ntchito zanu ndi chuma chanu,
8Wowononga adzabwera ndi kusakaza mzinda uliwonse,
9Mtsineni khutu Mowabu
10“Wotembereredwa munthu amene amagwira ntchito ya Yehova monyinyirika!
11“Mowabu wakhala pa mtendere kuyambira ubwana wake,
12Nʼchifukwa chake masiku akubwera,”
13Pamenepo Mowabu adzachita manyazi ndi Kemosi,
14“Kodi munganene bwanji kuti, ‘Ife ndife asilikali.
15Owononga Mowabu ndi mizinda yake abwera ndipo ankhondo adzalowa mʼmidzi yake;
16Kugwa kwa Mowabu kuli pafupi;
17Mulireni kwambiri, inu nonse amene mwamuzungulira,
18“Tsikani pa ulemerero wanu
19Inu amene mumakhala ku Aroeri,
20Iwo adzayankha kuti, “Mowabu wachititsidwa manyazi, pakuti wasakazika.
21Chiweruzo chabwera ku mizinda ya ku mapiri,
22Diboni, Nebo, Beti-Dibilataimu,
23Kiriyataimu, Beti-Gamuli, Beti-Meoni,
24Keriyoti ndi Bozira
25Mphamvu za Mowabu zawonongeka;
26“Muledzeretseni Mowabu,
27Kodi suja Israeli anali kwa iwe ngati chinthu chomachiseka?
28Inu amene mumakhala ku Mowabu,
29“Tamva za kunyada kwa Mowabu,
30Ine ndikuzidziwa ntchito zake,
31Nʼchifukwa chake ndidzamulira Mowabu,
32Ndikukhetsa misozi chifukwa cha inu, kupambana momwe ndinalirira Yazeri.
33Chimwemwe ndi chisangalalo zatha
34“A ku Hesiboni ndi Eleali akulira
35Ndidzawaletsa anthu a ku Mowabu
36“Nʼchifukwa chake mtima wanga ukulirira Mowabu ngati chitoliro.
37Aliyense wameta mutu wake
38Pa madenga onse a ku Mowabu
39“Taonani mmene waphwanyikira! Tamvani momwe akulirira!
40Yehova akuti,
41Mizinda idzagwidwa
42Mowabu sudzakhala mtundu wa anthu
43Zoopsa, dzenje ndi msampha zikudikira
44“Aliyense wothawa zoopsa
45“Anthu othawa nkhondo ayima pa mthunzi wa Hesiboni
46Tsoka kwa iwe Mowabu!
47“Komabe masiku akutsogolo