1Uthenga umene Yehova anamupatsa mneneri Yeremiya wonena za Afilisti, Farao asanathire nkhondo Gaza ndi uwu:
2Yehova akuti,
3akadzamva mgugu wa ngʼombe zazimuna zothamanga,
4Pakuti tsiku lafika
5Anthu a ku Gaza ameta mipala;
6“Mukulira kuti, ‘Aa, lupanga la Yehova,
7Koma lupangalo lidzapumula bwanji