We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yeremiya 47

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yeremiya 46 Yeremiya Yeremiya 48 →

1Uthenga umene Yehova anamupatsa mneneri Yeremiya wonena za Afilisti, Farao asanathire nkhondo Gaza ndi uwu:

2Yehova akuti,

3akadzamva mgugu wa ngʼombe zazimuna zothamanga,

4Pakuti tsiku lafika

5Anthu a ku Gaza ameta mipala;

6“Mukulira kuti, ‘Aa, lupanga la Yehova,

7Koma lupangalo lidzapumula bwanji

← Yeremiya 46 Yeremiya Yeremiya 48 →