1“Pitani uku ndi uku mʼmisewu ya Yerusalemu,
2Ngakhale anthu akulumbira kuti, ‘Pali Yehova wamoyo,’
3Inu Yehova, kodi suja mumafuna anthu onena zoona?
4Ndiye ndinati, “Awa ndi amphawi chabe;
5Tsono ndidzapita kwa atsogoleri
6Choncho mkango wochokera ku nkhalango udzawapha,
7Yehova akuti, “Kodi ndingakukhululukireni bwanji ndi zimene mwachita?
8Monga amachitira akavalo onenepa akamamemesa,
9Tsono ndingaleke kuwalanga chifukwa cha zimenezi?”
10“Pitani ku minda yake ya mipesa ndi kukayiwononga,
11Nyumba ya Israeli ndi nyumba ya Yuda
12Iwowa ankanama ponena za Yehova kuti,
13Mawu a aneneri azidzangopita ngati mphepo;
14Chifukwa chake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse akuti,
15Inu Aisraeli,” Yehova akuti,
16Zida zawo za nkhondo zapha anthu ambirimbiri;
17Adzakudyerani zokolola zanu ndi chakudya chanu,
18“Komabe pa masiku amenewo sindidzakuwonongani kotheratu,” akutero Yehova.
19Ndipo pamene anthu adzafunsa Yehova kuti, “Chifukwa chiyani Yehova Mulungu wathu wachita zimenezi?” Iwe udzawawuze kuti, “Monga momwe mwasiyira Ine ndi kutumikira milungu yachilendo mʼdziko mwanu, momwemonso mudzatumikira anthu a mʼdzikonso lachilendo.”
20“Lengeza izi kwa ana a Yakobo
21Imvani izi, inu anthu opusa ndi opanda nzeru,
22Kodi simuyenera kuchita nane mantha?”
23Koma anthu awa ndi nkhutukumve ndiponso a mitima yowukira;
24Sananenepo mʼmitima mwawo kuti,
25Koma zolakwa zanu zalepheretsa zonsezi;
26“Pakati pa anthu anga pali anthu ena oyipa
27Nyumba zawo zadzaza ndi chuma chochipeza mwa chinyengo
28Ndipo ananenepa ndi kukhala ndi matupi osalala.
29Kodi Ine ndingaleke kuwalanga chifukwa cha zimenezi?
30“Chinthu chothetsa nzeru ndi choopsa kwambiri
31Aneneri akunenera zabodza,