1“Thawani, inu anthu a ku Benjamini!
2Kodi mzinda wa Ziyoni suli ngati msipu wokongola kwambiri,
3Abusa ndi nkhosa zawo adzabwera kudzalimbana nawo;
4Adzanena kuti, “Konzekani kuwuthira nkhondo mzindawo!
5Tsono nyamukani kuti tiwuthire nkhondo mzindawu usiku uno
6Yehova Wamphamvuzonse akuti,
7Monga momwe chitsime chimatulutsira madzi
8Iwe Yerusalemu, tengapo phunziro,
9Yehova Wamphamvuzonse anandiwuza kuti,
10Kodi ndiyankhule ndi yani ndi kumuchenjeza?
11Koma ine ndadzazidwa ndi mkwiyo wa Yehova,
12Nyumba zawo adzazipereka kwa ena,
13“Kuyambira wamngʼono mpaka wamkulu,
14Amapoletsa zilonda za anthu anga
15Kodi amachita manyazi akamachita zonyansazo?
16Yehova akuti,
17Ine ndinakupatsani alonda oti akuyangʼanireni
18Nʼchifukwa chake imvani, inu anthu a mitundu ina;
19Imvani, inu anthu okhala pa dziko lapansi,
20Kodi pali phindu lanji ngakhale mubwere ndi lubani kuchokera ku Seba,
21Choncho Yehova akuti,
22Yehova akunena kuti,
23Atenga mauta ndi mikondo;
24A ku Ziyoni akuti “Ife tamva mbiri yawo,
25Musapite ku minda
26Inu anthu anga, valani ziguduli
27“Iwe Yeremiya, ndakuyika kuti ukhale choyesera zitsulo.
28Onsewo ali ndi khalidwe lokanika ndi lowukira
29Moto mu mvukuto ukuyaka kwambiri;
30Iwo ali ngati siliva wotayidwa,