1“Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraeli,
2Muzilumbira mokhulupirika ndiponso mwa chilungamo
3Zimene Yehova akunena kwa anthu a ku Yuda ndi a ku Yerusalemu ndi izi:
4Dziperekeni nokha kwa Ine
5“Lengeza ku Yuda ndi kulalikira mu Yerusalemu kuti,
6Kwezani mbendera kuyangʼana ku Ziyoni!
7Monga mkango umatulukira mʼngaka yake
8Choncho valani ziguduli,
9“Pa tsiku limenelo, mfumu ndi nduna zake adzataya mtima,
10Ndipo ine ndinati, “Haa, Ambuye Yehova, ndithu munawanyenga anthu awa pamodzi ndi Yerusalemu pamene munanena kuti, ‘Mudzakhala pa mtendere,’ chonsecho lupanga lili pakhosi pathu.”
11Nthawi imeneyo anthu awa ndi Yerusalemu adzawawuza kuti, “Mphepo yotentha yochokera ku magomo a mʼchipululu ikuwomba pa anthu anga, osati mphepo yopeta kapena yoyeretsa;
12koma mphepo yamphamvu kwambiri yochokera kwa Ine. Tsono ndi Ineyo amene ndikuwaweruza.”
13Taonani, adani akubwera ngati mitambo,
14Iwe Yerusalemu, tsuka mtima wako kuchotsa zoyipa kuti upulumuke.
15Pakuti amithenga akulalika mawu mʼdziko la Dani;
16Iwo akuti, “Fotokozani zimenezi kwa anthu a mitundu ina,
17Azinga Yerusalemu ngati anthu olondera munda,
18“Makhalidwe anu ndi zochita zanu
19Mayo, mayo,
20Tsoka limatsata tsoka linzake;
21Kodi ndikhale ndikuona mbendera ya nkhondo,
22Yehova akuti, “Anthu anga ndi zitsiru;
23Ndinayangʼana dziko lapansi,
24Ndinayangʼana mapiri,
25Ndinayangʼana, ndipo sindinaone anthu;
26Ndinayangʼana, dziko lachonde linali litasanduka chipululu;
27Yehova akuti,
28Chifukwa chake dziko lapansi lidzalira
29Pakumva phokoso la okwera pa akavalo ndi la anthu oponya mivi,
30Iwe Yerusalemu, ndiwe bwinja!
31Ndikumva kulira ngati kwa mayi pa nthawi yake yobereka,