1Lizani lipenga mu Ziyoni.
2tsiku la mdima ndi chisoni,
3Patsogolo pawo moto ukupsereza,
4Maonekedwe awo ali ngati akavalo;
5Akulumpha pamwamba pa mapiri
6Akangowaona, anthu a mitundu ina amazunzika mu mtima;
7Amathamanga ngati ankhondo;
8Iwo sakankhanakankhana,
9Amakhamukira mu mzinda,
10Patsogolo pawo dziko limagwedezeka,
11Yehova amabangula
12“Ngakhale tsopano,
13Ngʼambani mtima wanu
14Akudziwa ndani? Mwina adzasintha maganizo nʼkutimvera chisoni,
15Lizani lipenga mu Ziyoni,
16Sonkhanitsani anthu pamodzi,
17Ansembe amene amatumikira pamaso pa Yehova,
18Pamenepo Yehova adzachitira nsanje dziko lake
19Yehova adzawayankha kuti,
20“Ine ndidzachotsa ankhondo akumpoto kuti apite kutali ndi inu,
21Iwe dziko usachite mantha;
22Inu nyama zakuthengo, musachite mantha,
23Inu anthu a ku Ziyoni sangalalani,
24Pa malo opunthira padzaza tirigu;
25“Ine ndidzakubwezerani zonse zimene zinawonongedwa ndi dzombe,
26Mudzakhala ndi chakudya chambiri, mpaka mudzakhuta,
27Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine ndili mu Israeli,
28“Ndipo patapita nthawi,
29Ngakhalenso pa antchito anga aamuna ndi aakazi
30Ndidzaonetsa zodabwitsa mlengalenga
31Dzuwa lidzadetsedwa
32Ndipo aliyense amene adzayitana