We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yoweli 3

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yoweli 2 Yoweli

1“Masiku amenewo ndiponso nthawi imeneyo,

2ndidzasonkhanitsa anthu a mitundu yonse

3Anagawana anthu anga pochita maere

4“Kodi tsopano inu a ku Turo ndi Sidoni ndi madera onse a Filisitiya, muli ndi chiyani chotsutsana nane? Kodi mukundibwezera pa zinthu zimene ndakuchitirani? Ngati inu mukundibwezera, Ine ndidzabwezera zochita zanu mofulumira ndi mwachangu pa mitu yanu.

5Pakuti munatenga siliva ndi golide wanga ndi kupita nacho chuma changa chamtengowapatali ku nyumba zanu zopembedzera mafano.

6Inu munagulitsa anthu a ku Yuda ndi Yerusalemu kwa Agriki, kuti apite kutali ndi malire a dziko lawo.

7“Taonani, Ine ndidzawachotsa kumalo kumene munawagulitsako, ndipo ndidzabwezera zimene mwachita pa mitu yanu.

8Ndidzagulitsa ana anu aamuna ndi ana anu aakazi kwa anthu a ku Yuda, ndipo iwo adzawagulitsa kwa Aseba, mtundu wa anthu okhala kutali.” Yehova wayankhula.

9Lengezani izi pakati pa anthu a mitundu ina:

10Sulani makasu anu kuti akhale malupanga

11Bwerani msanga, inu anthu a mitundu yonse kuchokera ku mbali zonse,

12“Mitundu ya anthu idzuke;

13Tengani chikwakwa chodulira tirigu,

14Chigulu cha anthu, chigulu cha anthu,

15Dzuwa ndi mwezi zidzadetsedwa,

16Yehova adzabangula kuchokera mu Ziyoni

17“Pamenepo inu mudzadziwa kuti Ine Yehova Mulungu wanu,

18“Tsiku limenelo mapiri adzachucha vinyo watsopano,

19Koma Igupto adzasanduka bwinja,

20Koma Yuda adzakhala ndi anthu mpaka muyaya

21Kukhetsa magazi kwawo kumene Ine sindinakhululuke

← Yoweli 2 Yoweli