We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yoweli 1

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

Yoweli Yoweli 2 →

1Yehova anayankhula ndi Yoweli mwana wa Petueli.

2Inu akuluakulu, imvani izi;

3Muwafotokozere ana anu,

4Chimene dzombe losamera mapiko lasiya

5Dzukani, inu zidakwa ndipo mulire!

6Mtundu wa anthu wathira nkhondo dziko langa,

7Wawononga mphesa zanga

8Lirani ngati namwali wovala chiguduli,

9Chopereka cha chakudya ndi cha chakumwa

10Minda yaguga,

11Khalani ndi nkhawa, inu alimi,

12Mpesa wauma

13Inu ansembe, valani ziguduli ndipo lirani;

14Lengezani tsiku lopatulika losala zakudya,

15Kalanga ine tsikulo!

16Kodi chakudya chathu sichachotsedwa

17Mbewu zikunyala

18Taonani mmene zikulirira ziweto;

19Kwa Inu Yehova ndilirira,

20Ngakhale nyama zakuthengo zikulirira Inu;

Yoweli Yoweli 2 →