1Yehova anayankhula ndi Yoweli mwana wa Petueli.
2Inu akuluakulu, imvani izi;
3Muwafotokozere ana anu,
4Chimene dzombe losamera mapiko lasiya
5Dzukani, inu zidakwa ndipo mulire!
6Mtundu wa anthu wathira nkhondo dziko langa,
7Wawononga mphesa zanga
8Lirani ngati namwali wovala chiguduli,
9Chopereka cha chakudya ndi cha chakumwa
10Minda yaguga,
11Khalani ndi nkhawa, inu alimi,
12Mpesa wauma
13Inu ansembe, valani ziguduli ndipo lirani;
14Lengezani tsiku lopatulika losala zakudya,
15Kalanga ine tsikulo!
16Kodi chakudya chathu sichachotsedwa
17Mbewu zikunyala
18Taonani mmene zikulirira ziweto;
19Kwa Inu Yehova ndilirira,
20Ngakhale nyama zakuthengo zikulirira Inu;