We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 7

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 6 Yobu Yobu 8 →

1“Kodi munthu sakhala ndi ntchito yowawa pa dziko lapansi?

2Monga ngati kapolo wolakalaka mthunzi wa nthawi yamadzulo,

3choncho ine ndapatsidwa nthawi yongovutika pachabe,

4Ndikamagona ndimaganiza kuti, ‘Kodi kucha liti?’

5Thupi langa ladzala mphutsi ndi zipsera,

6“Masiku anga ndi othamanga kupambana makina wolukira nsalu,

7Inu Mulungu kumbukirani kuti moyo wanga uli ngati mpweya;

8Amene akundiona tsopano akundiona;

9Monga mtambo umazimirira ndi kukanganuka,

10Iye sadzabweranso ku nyumba kwake

11“Nʼchifukwa chake ine sindidzakhala chete;

12Kodi ine ndine nyanja kapena chirombo chamʼnyanja

13Pamene ndikuganiza kuti ndidzapeza chitonthozo pa bedi panga

14ngakhale nthawi imeneyo mumandiopseza ndi maloto

15kotero kuti ndimalakalaka kudzikhweza kapena kufa,

16Ine ndatopa nawo moyo wanga; sindingakonde kukhala moyo nthawi zonse.

17“Kodi munthu nʼchiyani kuti muzimuganizira chotere,

18kuti muzimusanthula mmawa uliwonse

19Kodi simudzaleka kumandizonda

20Ngati ine ndachimwa, ndachita chiyani kwa Inu,

21Chifukwa chiyani simukundikhululukira zolakwa zanga

← Yobu 6 Yobu Yobu 8 →