1“Itana ngati ungathe, koma ndani adzakuyankhe?
2Mkwiyo umapha chitsiru,
3Ine ndinaona chitsiru chitamera mizu,
4Ana ake alibe ndi chitetezo chomwe;
5Anthu anjala amamudyera zokolola zake,
6Pakuti masautso satuluka mʼfumbi,
7Komatu munthu amabadwira kuti azunzike
8“Koma ndikanakhala ine, ndikanamudandawulira Mulungu;
9Iye amachita zozizwitsa zimene sizimvetsetseka,
10Iye amagwetsa mvula pa dziko lapansi,
11Iye amakweza anthu wamba,
12Iyeyo amalepheretsa chiwembu cha anthu ochenjera,
13Iye amakola anthu ochenjera mu msampha wa kuchenjera kwawo,
14Mdima umawagwera nthawi yamasana;
15Mulungu amapulumutsa amphawi ku lupanga la mʼkamwa mwawo;
16Choncho osauka ali ndi chiyembekezo,
17“Wodala munthu amene Mulungu amamudzudzula;
18Pakuti Iye amavulaza koma amamanganso mabalawo;
19Pakuti adzakupulumutsa ku masautso nthawi ndi nthawi,
20Pa nthawi ya njala adzakulanditsa ku imfa,
21Adzakuteteza kwa anthu osinjirira,
22Uzidzaseka pa nthawi ya chiwonongeko ndi ya njala,
23Pakuti udzachita pangano ndi miyala ya mʼmunda mwako,
24Udzadziwa kuti nyumba yako ndi malo otetezedwa;
25Udzadziwa kuti ana ako adzakhala ambiri,
26Udzafika ku manda utakalamba,
27“Ife tafufuza zimenezi ndipo ndi zoona,