We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 30

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 29 Yobu Yobu 31 →

1“Koma tsopano akundinyoza,

2Kodi mphamvu zawo ndi za phindu lanji kwa ine,

3Anali atatheratu kuwonda ndi njala,

4Ankathyola therere ndi masamba owawa,

5Anapirikitsidwa pakati pa anthu anzawo,

6Anawumirizidwa kukhala ku zigwembe za mitsinje yowuma,

7Ankalira ngati nyama kuthengo

8Anali anthu achabechabe ndi wopanda dzina,

9“Ndipo tsopano ana awo akundiyimba nyimbo zachipongwe;

10Iwo amanyansidwa nane ndipo amandithawa;

11Tsopano pakuti Mulungu wakhwefula uta wanga ndipo wandisautsa,

12Ku dzanja langa lamanja anthu akulimbana nane;

13Iwo anditsekera njira;

14Akundithamangitsa ngati madzi olowera pa mpanda wobowoka,

15Zoopsa zandithetsa mphamvu;

16“Ndipo tsopano mtima wanga wachokamo;

17Mafupa anga akuphwanya usiku pakuti

18Mʼmphamvu zake Mulungu wakhala ngati chovala changa;

19Wandiponya mʼmatope,

20“Inu Mulungu, ine ndikulirira kwa Inu, koma simukundiyankha;

21Inuyo mumandichitira zankhanza;

22Mwandinyamulira ku mphepo ndipo mwandiwulutsa ndi mphepoyo;

23Ndikudziwa kuti Inu mudzandifikitsa ku imfa,

24“Ndithudi palibe munthu amene amalanga munthu wosweka mtima,

25Kodi ine sindinalire nawo iwo amene anali pamavuto?

26Koma pamene ndinkayembekezera zabwino, zoyipa ndiye zinandigwera;

27Kuwawa kwa mʼkati mwanga sikukuleka;

28Ndikuyenda wothimbirira, komatu osati ndi dzuwa;

29Ndasanduka mʼbale wa nkhandwe,

30Khungu langa layamba kuda ndipo likufunduka;

31Pangwe wanga wasanduka woyimbira maliro,

← Yobu 29 Yobu Yobu 31 →