We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 24

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 23 Yobu Yobu 25 →

1“Chifukwa chiyani Wamphamvuzonse sayikiratu nthawi yoti aweruze?

2Anthu amasuntha miyala ya mʼmalire, kuti akuze dziko lawo;

3Amalanda abulu a ana amasiye

4Amachotsa mʼmisewu anthu osauka,

5Amphawiwo amakhala ngati mbidzi mʼchipululu,

6Iwo amakolola za mʼminda ya eni ake,

7Amagona maliseche usiku wonse kusowa zovala;

8Amavumbwa ndi mvula ya mʼmapiri

9Amatsomphola mwana wamasiye wa ku bere;

10Amphawi amangoyenda maliseche kusowa zovala;

11Iwo amayenga mafuta a olivi mʼminda ya anthu oyipa;

12Kubuwula kwa anthu amene akufa kumamveka kuchokera mu mzinda,

13“Pali ena amene amakana kuwala,

14Dzuwa likalowa, wopha anzake amadzuka

15Munthu wachigololo amadikira chisisira;

16Mbala zimathyola nyumba usiku,

17Pakuti kwa onsewa mdima wandiweyani ndiye kuti kwawachera.

18“Komatu iwowo ndi thovu loyandama pa madzi;

19Monga momwe kutentha ndi chilala zimasungunulira madzi owundana

20Mayi wowabereka amawayiwala,

21Amachitira nkhanza mayi wosabala ndi mayi amene alibe mwana,

22Koma Mulungu amawononga munthu wamphamvu mwa mphamvu zake;

23Mulungu atha kuwalola kuti akhale mosatekeseka,

24Kwa kanthawi kochepa oyipa amakwezedwa ndipo kenaka saonekanso;

25“Ngati zimenezi sizoona, ndani angaonetse kuti ndine wabodza

← Yobu 23 Yobu Yobu 25 →