We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yobu 23

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yobu 22 Yobu Yobu 24 →

1Pamenepo Yobu anayankha kuti,

2“Leronso kudandaula kwanga nʼkwakukulu kwambiri;

3Ndikanangodziwa kumene ndikanamupeza Mulungu;

4Ndikanafotokoza mlandu wanga pamaso pake

5Ndikanadziwa mawu amene Iye akanandiyankha,

6Kodi Iye akanalimbana nane mwa mphamvu zake zazikulu?

7Kumeneko munthu wolungama akanafotokoza mlandu wake pamaso pake,

8“Taonani, ndikapita kummawa, Iye kulibe kumeneko,

9Akamagwira ntchito kumpoto, sindimuona kumeneko

10Koma Iye amadziwa mmene ndimayendera;

11Mapazi anga akhala akuponda mʼmapazi ake;

12Sindinapatuke kusiya malamulo ochokera pakamwa pake;

13“Koma Iyeyo ndi wosasinthika, ndipo ndani angatsutsane naye?

14Iye amachita chimene watsimikiza kuti chindichitikire,

15Nʼchifukwa chake ndikuchita mantha kwambiri pamaso pake;

16Mulungu walefula mtima wanga;

17Komatu sindinachititsidwe mantha ndi mdima,

← Yobu 22 Yobu Yobu 24 →