1Apo Bilidadi wa ku Suki anayankha kuti,
2“Ulamuliro ndi kuopsa ndi za Mulungu,
3Kodi magulu ake ankhondo nʼkuwerengeka?
4Kodi munthu angakhale bwanji wolungama pamaso pa Mulungu?
5Ngati mwezi sutha kuwala kwenikweni,
6nanji tsono munthu amene ali ngati mphutsi,