1Inu Yehova, bwanji mukanangongʼamba mlengalenga ndi kutsika pansi,
2Monga momwe moto umatenthera tchire
3Pakuti nthawi ina pamene munatsika munachita zinthu zoopsa zimene sitinaziyembekezere,
4Chikhalire palibe ndi mmodzi yemwe anamvapo
5Inu mumabwera kudzathandiza onse amene amakondwera pochita zolungama,
6Tonsefe takhala ngati anthu amene ndi odetsedwa,
7Palibe amene amapemphera kwa Inu
8Komabe, Inu Yehova ndinu Atate athu.
9Inu Yehova, musatikwiyire kopitirira muyeso
10Mizinda yanu yopatulika yasanduka chipululu;
11Nyumba yanu yopatulika ndi yaulemu, kumene makolo athu ankakutamandani,
12Inu Yehova, zonse zachitikazi, kodi mungokhala osatithandiza?