1“Ndinali wokonzeka kumva mapemphero a amene sankandipempha kanthu;
2Tsiku lonse ndatambasulira manja anga
3Ndatambasulira manja anga anthu aja amene nthawi zonse amandikwiyitsa
4Amakatandala ku manda
5Amawuza ena kuti, ‘Khala patali usandiyandikire,
6“Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo;
7ndi a makolo awo,”
8Yehova akuti,
9Ndidzatulutsa zidzukulu mʼbanja la Yakobo,
10Chigwa cha Saroni chidzakhala kodyetserako nkhosa,
11“Koma inu amene mumasiya Yehova
12ndidzakuperekani ku lupanga ngati nsembe,
13Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti,
14Atumiki anga adzayimba
15Anthu anga osankhidwa
16Aliyense wopempha dalitso mʼdzikomo
17“Taonani, ndikulenga
18Koma inu mukhale osangalala ndi okondwa mpaka muyaya
19Ine ndidzakondwa chifuwa cha Yerusalemu
20“Ana sadzafa ali akhanda
21Anthu adzamanga nyumba ndi kukhalamo,
22Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo,
23Sadzagwira ntchito pachabe
24Ndidzawayankha ngakhale asanathe nʼkupempha komwe.
25Mʼmbulu ndi mwana wankhosa wamkazi zidzadyera pamodzi.