We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 65

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 64 Yesaya Yesaya 66 →

1“Ndinali wokonzeka kumva mapemphero a amene sankandipempha kanthu;

2Tsiku lonse ndatambasulira manja anga

3Ndatambasulira manja anga anthu aja amene nthawi zonse amandikwiyitsa

4Amakatandala ku manda

5Amawuza ena kuti, ‘Khala patali usandiyandikire,

6“Taonani, ndatsimikiza kale mlandu ndi chilango chawo;

7ndi a makolo awo,”

8Yehova akuti,

9Ndidzatulutsa zidzukulu mʼbanja la Yakobo,

10Chigwa cha Saroni chidzakhala kodyetserako nkhosa,

11“Koma inu amene mumasiya Yehova

12ndidzakuperekani ku lupanga ngati nsembe,

13Nʼchifukwa chake Ambuye Yehova akuti,

14Atumiki anga adzayimba

15Anthu anga osankhidwa

16Aliyense wopempha dalitso mʼdzikomo

17“Taonani, ndikulenga

18Koma inu mukhale osangalala ndi okondwa mpaka muyaya

19Ine ndidzakondwa chifuwa cha Yerusalemu

20“Ana sadzafa ali akhanda

21Anthu adzamanga nyumba ndi kukhalamo,

22Sadzamanganso nyumba anthu ena nʼkukhalamo,

23Sadzagwira ntchito pachabe

24Ndidzawayankha ngakhale asanathe nʼkupempha komwe.

25Mʼmbulu ndi mwana wankhosa wamkazi zidzadyera pamodzi.

← Yesaya 64 Yesaya Yesaya 66 →