1“Dzuka, wala, pakuti kuwala kwako kwafika,
2Taona, mdima waphimba dziko lapansi
3Mitundu ya anthu idzatsata kuwunika kwako
4“Tukula maso ako, yangʼanayangʼana ndipo ona zimene zikuchitika.
5Ukadzaona zimenezi udzasangalala kwambiri,
6Gulu la ngamira lidzaphimba dziko lako,
7Ziweto zonse za ku Kedara adzazisonkhanitsa kwa inu,
8“Kodi ndi zayani izo zikuwuluka ngati mitambo,
9Ndithu, izi ndi sitima za pa madzi zochokera ku mayiko akutali;
10“Alendo adzamanganso malinga ako,
11Zipata zako zidzakhala zotsekula nthawi zonse,
12Pakuti mtundu wa anthu ndi mafumu amene sakutumikira iwe;
13“Adzabwera nayo kwa iwe mitengo ya payini,
14Ana aja amene anakuzunzani adzabwera ndipo adzakugwadirani;
15“Ngakhale anthu anakusiya nadana nawe,
16Udzamwa mkaka wa mitundu ya anthu
17Ndidzakupatsa golide mʼmalo mwa mkuwa,
18Ziwawa sizidzamvekanso mʼdziko lako,
19Sipadzakhala dzuwa kuti likuwunikire,
20Dzuwa lako silidzalowanso,
21Ndipo anthu ako onse adzakhala olungama
22Kabanja kakangʼono kadzasanduka fuko,