1Taonani, mkono wa Yehova si waufupi kuti sungathe kupulumutsa,
2Koma zoyipa zanu zakulekanitsani
3Pakuti manja anu ali psuu ndi magazi.
4Palibe amene akuyimba mnzake mlandu molungama,
5Iwo amayikira mazira a mamba
6Ukonde wawo wa kangawude sangawuvale ngati chovala;
7Amathamangira kukachita zoyipa;
8Iwo sadziwa kuchita za mtendere;
9Anthu akuti, “Chifukwa cha zimenezi chilungamo chatitalikira;
10Timapapasapapasa khoma ngati munthu wosaona,
11Tonse timabangula ngati zimbalangondo:
12Pakuti zolakwa zathu nʼzochuluka pamaso panu,
13Tawukira ndi kumukana Yehova.
14Motero kuweruza kolungama kwalekeka
15Choonadi sichikupezeka kumeneko,
16Yehova anaona kuti panalibe ndi mmodzi yemwe,
17Iye anavala chilungamo ngati chovala chachitsulo chapachifuwa,
18Iye adzawabwezera chilango adani a anthu ake
19Choncho akadzabwera ngati madzi
20“Mpulumutsi adzabwera ku Ziyoni
21Yehova akuti, “Kunena za pangano lake ndi iwo, Mzimu wanga umene uli pa inu, ndiponso mawu anga amene ndayika mʼkamwa mwanu sadzachoka mʼkamwa mwanu, kapena kuchoka mʼkamwa mwa ana anu, kapena mʼkamwa mwa zidzukulu zawo kuyambira tsopano mpaka kalekale,”