1“Fuwula kwambiri, usaleke.
2Pakuti tsiku ndi tsiku amafunafuna Ine;
3Anthu akufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani ife tasala
4Mumati uku mukusala kudya, uku mukukangana ndi kumenyana,
5Kodi kusala kudya kumene ndimakufuna Ine nʼkumeneku,
6“Kodi si uku kusala kudya kumene Ine ndimakufuna:
7Anthu anjala kodi mwawagawira chakudya chanu?
8Mukatero chipulumutso chanu chidzabwera ngati mʼbandakucha,
9Mukamadzapemphera Yehova adzakuyankhani;
10Ndipo ngati mudyetsa anthu anjala,
11Yehova adzakutsogolerani nthawi zonse;
12Anthu ako adzamanganso nyumba zimene zakhala mabwinja nthawi yayitali,
13“Muzisunga osaphwanya Sabata;
14mukatero mudzapeza chimwemwe mwa Yehova,