We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 58

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 57 Yesaya Yesaya 59 →

1“Fuwula kwambiri, usaleke.

2Pakuti tsiku ndi tsiku amafunafuna Ine;

3Anthu akufunsa kuti, ‘Chifukwa chiyani ife tasala

4Mumati uku mukusala kudya, uku mukukangana ndi kumenyana,

5Kodi kusala kudya kumene ndimakufuna Ine nʼkumeneku,

6“Kodi si uku kusala kudya kumene Ine ndimakufuna:

7Anthu anjala kodi mwawagawira chakudya chanu?

8Mukatero chipulumutso chanu chidzabwera ngati mʼbandakucha,

9Mukamadzapemphera Yehova adzakuyankhani;

10Ndipo ngati mudyetsa anthu anjala,

11Yehova adzakutsogolerani nthawi zonse;

12Anthu ako adzamanganso nyumba zimene zakhala mabwinja nthawi yayitali,

13“Muzisunga osaphwanya Sabata;

14mukatero mudzapeza chimwemwe mwa Yehova,

← Yesaya 57 Yesaya Yesaya 59 →