1Mzimu wa Ambuye Yehova uli pa ine,
2Wandituma kuti ndikalengeze nthawi imene Yehova adzapulumutsa anthu ake;
3Wandituma kuti ndiwakonzere olira a ku Ziyoni,
4Adzamanganso mabwinja akale a mzinda
5Anthu achilendo adzakutumikirani; adzazidyetsa ziweto zanu;
6Ndipo inu mudzatchedwa ansembe a Yehova,
7Chifukwa manyazi awo anali owirikiza;
8“Pakuti Ine Yehova, ndimakonda chilungamo;
9Ana awo adzakhala odziwika pakati pa mitundu ya anthu
10Ine ndikusangalala kwambiri chifukwa cha Yehova;
11Monga momwe nthaka imameretsa mbewu