We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 61

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 60 Yesaya Yesaya 62 →

1Mzimu wa Ambuye Yehova uli pa ine,

2Wandituma kuti ndikalengeze nthawi imene Yehova adzapulumutsa anthu ake;

3Wandituma kuti ndiwakonzere olira a ku Ziyoni,

4Adzamanganso mabwinja akale a mzinda

5Anthu achilendo adzakutumikirani; adzazidyetsa ziweto zanu;

6Ndipo inu mudzatchedwa ansembe a Yehova,

7Chifukwa manyazi awo anali owirikiza;

8“Pakuti Ine Yehova, ndimakonda chilungamo;

9Ana awo adzakhala odziwika pakati pa mitundu ya anthu

10Ine ndikusangalala kwambiri chifukwa cha Yehova;

11Monga momwe nthaka imameretsa mbewu

← Yesaya 60 Yesaya Yesaya 62 →