1Yehova akuti,
2Ndi wodala munthu amene amachita zimenezi,
3Mlendo amene waphatikana ndi Yehova asanene kuti,
4Popeza Yehova akuti,
5ndidzawapatsa dzina ndi mbiri yabwino
6Yehova akuti, “Alendo amene amadziphatika kwa Yehova,
7amenewa Ine ndidzawafikitsa ku phiri langa lopatulika,
8Ambuye Yehova, amene amasonkhanitsa
9Bwerani, inu zirombo zonse zakuthengo,
10Atsogoleri onse a Israeli ndi akhungu,
11Ali ngati agalu amene ali ndi njala yayikulu;
12Aliyense amafuwulira mnzake kuti, “Bwera, tiye timwe vinyo!