We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 55

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 54 Yesaya Yesaya 56 →

1“Bwerani, inu nonse amene muli ndi ludzu,

2Chifukwa chiyani ndalama zanu mukuwonongera zinthu zimene samadya,

3Tcherani makutu ndipo mubwere kwa Ine;

4Taonani, ine ndamusankha kuti akhale mboni yanga kwa mitundu ya anthu,

5Ndithu inu mudzayitanitsa mitundu ya anthu imene simuyidziwa,

6Funafunani Yehova pamene Iye akupezeka.

7Woyipa asiye makhalidwe ake oyipa,

8“Pakuti maganizo anga siwofanana ndi maganizo anu,

9“Monga momwe mlengalenga muli kutali ndi dziko lapansi,

10Monga mvula ndi chisanu chowundana

11Ndi mmenenso amachitira mawu ochokera mʼkamwa mwanga.

12Inu mudzatuluka mu mzindawo mwachimwemwe

13Mʼmalo mʼmene tsopano muli mitengo ya minga mudzamera mitengo ya payini,

← Yesaya 54 Yesaya Yesaya 56 →