1“Sangalala, iwe mayi wosabala,
2Kulitsa malo omangapo tenti yako,
3Pakuti udzasendeza malire ako kumanja ndi kumanzere;
4“Usachite mantha; sadzakunyozanso.
5Pakuti Mlengi wako ali ngati mwamuna wako,
6Yehova wakuyitananso,
7“Kwa kanthawi kochepa, Ine ndinakusiya,
8Ndinakufulatira kwa kanthawi kochepa
9“Kwa ine zimenezi zili ngati mmene zinalili mʼnthawi ya Nowa.
10Ngakhale mapiri atagwedezeka
11“Iwe mzinda wozunzika, wokunthidwa ndi namondwe ndiponso wopanda wokutonthoza,
12Ndidzamanga nsanja zako zankhondo ndi miyala yokongola ya rubi.
13Yehova adzaphunzitsa ana ako onse,
14Udzakhazikika mʼchilungamo chenicheni:
15Ngati wina adzakuthirani nkhondo, si ndine amene ndachititsa;
16“Taona, ndi Ine amene ndinalenga munthu wosula zitsulo
17palibe chida chopangidwa ndi mdani chimene chidzakupweteke,