We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 53

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 52 Yesaya Yesaya 54 →

1Ndani wakhulupirira zimene tanenazi;

2Iye anakula ngati mphukira pamaso pake,

3Iye ananyozedwa ndi kukanidwa ndi anthu,

4Ndithudi, iye anamva zowawa mʼmalo mwa ife;

5Koma iye analasidwa chifukwa cha zolakwa zathu,

6Ife tonse, ngati nkhosa, tasochera,

7Anthu anamuzunza ndi kumusautsa,

8Atatha kumugwira mwankhanza ndikumuyimba mlandu, kenaka anapita naye kukamupha.

9Anamukonzera manda ake pamodzi ndi anthu oyipa

10Komatu ndi Yehova amene anafuna kuti amuzunze ndi kumusautsa.

11Atatha mazunzo a moyo wake,

12Motero Ine ndidzamupatsa ulemu pamodzi ndi akuluakulu,

← Yesaya 52 Yesaya Yesaya 54 →