1Dzambatuka, dzambatuka iwe Ziyoni,
2Sasa fumbi lako;
3Pakuti Yehova akuti,
4Pakuti Ambuye Yehova akuti,
5Tsopano Ine Yehova ndikuti,
6Tsono tsiku limenelo anthu anga adzadziwa dzina langa;
7Ngokongoladi mapazi a
8Mverani! Alonda anu akukweza mawu awo;
9Imbani pamodzi mofuwula nyimbo zachimwemwe,
10Yehova wagwiritsa ntchito mphamvu zake zopatulika
11Nyamukani, nyamukani, chokaniko ku Babuloniko!
12Koma simudzachoka mofulumira
13Taonani, mtumiki wanga adzapambana pa ntchito yake
14Anthu ambiri atamuona anadzidzimuka,
15Momwemonso anthu a mitundu yonse adzadodoma naye,