1“Mverani Ine, inu amene mukufuna chipulumutso
2taganizani za Abrahamu, kholo lanu,
3Yehova adzatonthozadi Ziyoni,
4“Mverani Ine, anthu anga:
5Ndili pafupi kubwera kudzawombola anthu anga.
6Kwezani maso anu mlengalenga,
7“Mverani Ine, inu amene mukudziwa choonadi,
8Pakuti njenjete idzawadya ngati chovala;
9Dzambatukani, dzambatukani! Valani zilimbe,
10Kodi sindinu amene munawumitsa nyanja yayikulu,
11Anthu amene Yehova anawawombola adzabwerera
12Yehova akuti, “Ndinetu amene ndimakutonthozani mtima.
13Koma inu mumayiwala Yehova Mlengi wanu,
14Amʼndende adzamasulidwa posachedwa;
15Pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu,
16Ndayika mawu anga mʼkamwa mwanu
17Dzambatuka, dzambatuka!
18Mwa ana onse amene anabereka,
19Mavuto awiriwa akugwera iwe.
20Ana ako akomoka;
21Nʼchifukwa chake imva izi iwe amene ukuvutika,
22Ambuye Yehova wanu,
23Ndidzapereka chikhocho kwa anthu amene amakuzunza,