1Yehova akuti,
2Nʼchifukwa chiyani pamene ndinabwera kudzakupulumutsani panalibe munthu?
3Ndinaphimba thambo ndi mdima
4Ambuye Yehova anandiphunzitsa mawu oyenera kuyankhula
5Ambuye Yehova wanditsekula makutu anga,
6Ndinapereka msana wanga kwa ondimenya
7Popeza Ambuye Yehova amandithandiza,
8Wondikhalira kumbuyo ali pafupi,
9Ambuye Yehova ndiye amene amandithandiza.
10Ndani mwa inu amaopa Yehova
11Koma tsopano inu nonse amene mumasonkha moto