We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 50

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 49 Yesaya Yesaya 51 →

1Yehova akuti,

2Nʼchifukwa chiyani pamene ndinabwera kudzakupulumutsani panalibe munthu?

3Ndinaphimba thambo ndi mdima

4Ambuye Yehova anandiphunzitsa mawu oyenera kuyankhula

5Ambuye Yehova wanditsekula makutu anga,

6Ndinapereka msana wanga kwa ondimenya

7Popeza Ambuye Yehova amandithandiza,

8Wondikhalira kumbuyo ali pafupi,

9Ambuye Yehova ndiye amene amandithandiza.

10Ndani mwa inu amaopa Yehova

11Koma tsopano inu nonse amene mumasonkha moto

← Yesaya 49 Yesaya Yesaya 51 →