1Mverani Ine, inu anthu a pa zilumba
2Iye anasandutsa pakamwa panga kukhala ngati lupanga lakuthwa,
3Iye anati kwa ine, “Ndiwe mtumiki wanga, Israeli.
4Koma Ine ndinati, “Ine ndinkaganiza kuti ndinagwira ntchito
5Yehova anandiwumba ine
6Yehovayo tsono akuti,
7Yehova Mpulumutsi ndi Woyerayo wa Israeli akuyankhula,
8Yehova akuti,
9Ndidzawuza a mʼndende kuti atuluke
10Iwo sadzamva njala kapena ludzu,
11Mapiri anga onse ndidzawasandutsa njira yoyendamo,
12Taonani, anthu anga adzachokera kutali,
13Imbani mwachimwemwe, inu zolengedwa zamlengalenga;
14Koma Ziyoni anati, “Yehova wandisiya,
15“Kodi amayi angathe kuyiwala mwana wawo wakubere
16Taona, ndakulemba iwe mʼzikhantho zanga;
17Amisiri odzakumanganso akubwerera mofulumira,
18Kweza maso ako ndipo uyangʼaneyangʼane
19“Ngakhale unasanduka bwinja ndi kuwonongedwa
20Ana obadwa nthawi yako yachisoni
21Tsono iwe udzadzifunsa kuti,
22Zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi,
23Mafumu adzakhala abambo wongokulera
24Kodi mungathe kulanda anthu ankhondo zofunkha zawo,
25Koma zimene Yehova akunena ndi izi,
26Anthu amene anakuponderezani adzadya mnofu wawo omwe;