We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 49

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 48 Yesaya Yesaya 50 →

1Mverani Ine, inu anthu a pa zilumba

2Iye anasandutsa pakamwa panga kukhala ngati lupanga lakuthwa,

3Iye anati kwa ine, “Ndiwe mtumiki wanga, Israeli.

4Koma Ine ndinati, “Ine ndinkaganiza kuti ndinagwira ntchito

5Yehova anandiwumba ine

6Yehovayo tsono akuti,

7Yehova Mpulumutsi ndi Woyerayo wa Israeli akuyankhula,

8Yehova akuti,

9Ndidzawuza a mʼndende kuti atuluke

10Iwo sadzamva njala kapena ludzu,

11Mapiri anga onse ndidzawasandutsa njira yoyendamo,

12Taonani, anthu anga adzachokera kutali,

13Imbani mwachimwemwe, inu zolengedwa zamlengalenga;

14Koma Ziyoni anati, “Yehova wandisiya,

15“Kodi amayi angathe kuyiwala mwana wawo wakubere

16Taona, ndakulemba iwe mʼzikhantho zanga;

17Amisiri odzakumanganso akubwerera mofulumira,

18Kweza maso ako ndipo uyangʼaneyangʼane

19“Ngakhale unasanduka bwinja ndi kuwonongedwa

20Ana obadwa nthawi yako yachisoni

21Tsono iwe udzadzifunsa kuti,

22Zimene Ambuye Yehova akunena ndi izi,

23Mafumu adzakhala abambo wongokulera

24Kodi mungathe kulanda anthu ankhondo zofunkha zawo,

25Koma zimene Yehova akunena ndi izi,

26Anthu amene anakuponderezani adzadya mnofu wawo omwe;

← Yesaya 48 Yesaya Yesaya 50 →