1“Mverani izi, inu nyumba ya Yakobo,
2Komabe inu mumadzitcha nzika za mzinda wopatulika
3Zimene zinachitika poyamba ndinalosera kalekale,
4Pakuti Ine ndinadziwa kuti iwe ndiwe nkhutukumve
5Ine ndinakuwuziratu zinthu izi kalekale lomwe;
6Inu munamva zinthu zimenezi.
7Zinthu zimenezi zikulengedwa tsopano lino, osati kalekale;
8Inu simunazimvepo kapena kuzidziwa;
9Ine ndikuchedwetsa mkwiyo wanga chifukwa cha dzina langa.
10Taonani, ndinakuyeretsani ngati siliva;
11Chifukwa cha ulemu wanga, chifukwa cha ulemu wanga Ine ndikuchita zimenezi.
12“Tamvera Ine, iwe Yakobo,
13Inde dzanja langa linamanga maziko a dziko lapansi,
14“Sonkhanani pamodzi inu nonse ndipo mvetserani:
15Ine, Inetu, ndayankhula;
16“Bwerani pafupi ndipo mvetserani izi:
17Yehova, Mpulumutsi wanu,
18Ngati iwe ukanangosamalira zolamulira zanga,
19Zidzukulu zako zikanachuluka ngati mchenga,
20Tulukani mʼdziko la Babuloni!
21Iwo sanamve ludzu pamene Yehova ankawatsogolera mʼchipululu;
22“Palibe mtendere kwa anthu ochimwa,” akutero Yehova.