1“Tsika, ndi kukhala pa fumbi,
2Tenga mphero ndipo upere ufa;
3Maliseche ako adzakhala poyera
4Woyerayo wa Israeli ndiye Mpulumutsi wathu,
5“Khala chete, ndipo lowa mu mdima,
6Ndinawakwiyira anthu anga,
7Iwe unati, ‘Ine ndidzakhalapo nthawi zonse
8“Ndipo tsopano, tamvera, iwe wongokonda zokondweretsawe,
9Koma mʼkamphindi, ndiponso tsiku limodzi,
10Iwe unkadalira kuyipa kwako
11Ngozi yayikulu idzakugwera
12“Pitiriza tsono kukhala ndi matsenga ako,
13Malangizo onse amene unalandira angokutopetsa basi!
14Ndithudi, anthuwo ali ngati phesi;
15Umu ndi mmene adzachitire amatsenga,