We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 46

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 45 Yesaya Yesaya 47 →

1Beli wagwada pansi, Nebo wawerama;

2Nyamazo zikuwerama ndi kufuna kugwa ndi milunguyo;

3Mverani Ine, Inu nyumba ya Yakobo,

4Mpaka pamene mudzakalambe ndi kumera imvi

5“Kodi inu mudzandifanizira ndi yani, kapena mufananitsa ndi yani?

6Anthu ena amakhuthula golide mʼzikwama zawo

7Amanyamula nʼkumayenda nayo milunguyo pa mapewa awo;

8“Kumbukirani zimenezi ndipo muchite manyazi,

9Kumbukirani zinthu zakale zinthu zamakedzana;

10Ndinaneneratu zakumathero kuchokera pachiyambi pomwe.

11Ndikuyitana chiwombankhanga kuchokera kummawa.

12Ndimvereni, inu anthu owuma mtima,

13Ndikubweretsa pafupi tsiku la chipulumutso changa;

← Yesaya 45 Yesaya Yesaya 47 →