1Yehova akuyankhula ndi wodzozedwa wake
2Ine ndidzayenda patsogolo pako,
3Ndidzakupatsa chuma chobisika mu mdima,
4Chifukwa cha mtumiki wanga Yakobo,
5Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina;
6kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo
7Ndimalenga kuwala ndi mdima,
8“Iwe thambo gwetsa mvula kuchokera kumwamba;
9“Tsoka kwa wokangana ndi mlengi wake,
10Tsoka kwa wofunsa abambo ake kuti,
11“Yehova
12Ndine amene ndinapanga dziko lapansi
13Ndine amene ndidzawutsa Koresi kuti chilungamo changa chikwaniritsidwe:
14Yehova akuti,
15Zoonadi inu muli ndi Mulungu wobisika
16Onse amene amapanga mafano adzawachititsa manyazi ndi kuwanyozetsa.
17Koma Yehova adzapulumutsa Israeli
18Yehova
19Ine sindinayankhule mwachinsinsi,
20Yehova akuti, “Sonkhanani pamodzi ndipo mubwere;
21Fotokozani mlandu wanu,
22“Tembenukirani kwa Ine kuti mupulumuke,
23Ndalumbira ndekha,
24Iwo adzanene kwa Ine kuti,
25Koma mwa Yehova zidzukulu zonse za Israeli