We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 45

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 44 Yesaya Yesaya 46 →

1Yehova akuyankhula ndi wodzozedwa wake

2Ine ndidzayenda patsogolo pako,

3Ndidzakupatsa chuma chobisika mu mdima,

4Chifukwa cha mtumiki wanga Yakobo,

5Ine ndine Yehova ndipo palibenso wina;

6kotero kuti kuchokera kummawa mpaka kumadzulo

7Ndimalenga kuwala ndi mdima,

8“Iwe thambo gwetsa mvula kuchokera kumwamba;

9“Tsoka kwa wokangana ndi mlengi wake,

10Tsoka kwa wofunsa abambo ake kuti,

11“Yehova

12Ndine amene ndinapanga dziko lapansi

13Ndine amene ndidzawutsa Koresi kuti chilungamo changa chikwaniritsidwe:

14Yehova akuti,

15Zoonadi inu muli ndi Mulungu wobisika

16Onse amene amapanga mafano adzawachititsa manyazi ndi kuwanyozetsa.

17Koma Yehova adzapulumutsa Israeli

18Yehova

19Ine sindinayankhule mwachinsinsi,

20Yehova akuti, “Sonkhanani pamodzi ndipo mubwere;

21Fotokozani mlandu wanu,

22“Tembenukirani kwa Ine kuti mupulumuke,

23Ndalumbira ndekha,

24Iwo adzanene kwa Ine kuti,

25Koma mwa Yehova zidzukulu zonse za Israeli

← Yesaya 44 Yesaya Yesaya 46 →