1Yehova akuti, “Mvera tsopano, iwe Yakobo, mtumiki wanga,
2Yehova
3Pakuti ndidzathira madzi pa nthaka yowuma,
4Iwo adzakula ngati udzu wothirira bwino
5Wina adzanena kuti, ‘Ine ndine wa Yehova;’
6“Yehova Mfumu
7Ndani nanga angafanane ndi Ine? Muloleni kuti ayankhule.
8Musanjenjemere, musachite mantha.
9Onse amene amapanga mafano ngachabe,
10Ndani amasema mulungu ndi kuwumba fano,
11Iye pamodzi ndi anzake onse adzawachititsa manyazi;
12Mmisiri wa zitsulo amatenga chitsulo
13Mmisiri wa matabwa nayenso amayeza mtengo ndi chingwe
14Amagwetsa mitengo ya mkungudza,
15Mitengoyo munthu amachitako nkhuni;
16Chigawo china cha mtengowo amasonkhera moto
17Chigawo chotsala amapanga kamulungu, fano lake limenelo;
18Anthu otere sadziwa kanthu, samvetsa kanthu kalikonse;
19Palibe amene amayima nʼkulingalira.
20Munthu wotere ali ngati wodya phulusa, maganizo ake opusa amusocheretsa;
21Yehova akuti, “Iwe Yakobo, kumbukira zinthu izi
22Ndachotsa zolakwa zako ngati mitambo,
23Imbani mwachimwemwe, inu zolengedwa zamlengalenga, pakuti Yehova wachita zimenezi;
24Yehova Mpulumutsi wanu, amene
25Ndine amene ndinalepheretsa mipingo ya anthu onyenga,
26Ndine amene ndimatsimikiza mawu a atumiki ake
27Ndine amene ndinawuza nyanga yayikulu kuti, ‘Uma’
28Ndine amene ndinanena kwa Koresi kuti, ‘Iye ndiye mʼbusa wanga,’