1Koma tsopano, Yehova
2Pamene ukuwoloka nyanja,
3Chifukwa Ine Yehova, Mulungu wako,
4Popeza kuti ndiwe wamtengowapatali wolemekezeka ndi wapamtima panga,
5Usachite mantha, pakuti Ine ndili nawe;
6Ndidzawuza a kumpoto kuti, ‘Amasuleni,’
7onsewo amadziwika ndi dzina langa;
8Tulutsa anthu amene ali nawo maso koma sakupenya,
9Mitundu yonse ya anthu isonkhane pamodzi,
10Yehova akunena kuti, “Inu Aisraeli ndinu mboni zanga,
11Akutero Yehova, “Ine, Inetu ndine Yehova,
12Ndine amene ndinaneneratu, amene ndinakupulumutsa;
13“Ine ndine Mulungu kuyambira nthawi yamakedzana, ndipo ndidzakhalabe Mulungu ku nthawi zonse.
14Yehova akuti,
15Ine ndine Yehova, Woyera wanu uja,
16Yehova
17Iye anasonkhanitsa magaleta, akavalo,
18“Iwalani zinthu zakale;
19Taonani, Ine ndikuchita zinthu zatsopano!
20Nyama zakuthengo, nkhandwe ndi akadzidzi
21Anthu amene ndinadziwumbira ndekha
22“Komatu simunapemphera kwa Ine, Inu a mʼbanja la Yakobo,
23Simunabweretse kwa Ine nkhosa za nsembe zopsereza,
24Simunandigulire bango lonunkhira
25“Ine, Inetu, ndi amene ndimafafaniza
26Mundikumbutse zakale,
27Kholo lanu loyamba linachimwa;
28Chifukwa chake Ine ndidzanyazitsa akuluakulu a Nyumba yanu ya mapemphero,