1“Nayu mtumiki wanga, amene ndimamuchirikiza,
2Iye sadzafuwula, sadzamveka mawu,
3Bango lophwanyika sadzalithyola,
4sadzafowoka kapena kukhumudwa
5Yehova Mulungu
6“Ine Yehova, ndakuyitana chifukwa Ine ndine wolungama;
7Udzatsekula maso a anthu osaona,
8“Ine ndine Yehova: dzina langa ndi limenelo!
9Taonani, zinthu zimene ndinalosera kale zachitikadi,
10Imbirani Yehova nyimbo yatsopano,
11Chipululu ndi mizinda yake zikweze mawu awo;
12Atamande Yehova
13Yehova adzapita ku nkhondo ngati munthu wamphamvu,
14Yehova akuti, “Ndakhala ndili chete kwa nthawi yayitali,
15Ndidzawononga mapiri ndi zitunda
16Ndidzatsogolera anthu osaona mʼmisewu imene sanayidziwe,
17Koma onse amene amadalira mafano
18“Imvani, agonthi inu;
19Ali wosaona ndani, si mtumiki wanga kodi?
20Iwe waona zinthu zambiri, koma sunazisamale;
21Chinamukomera Yehova
22Koma awa ndi anthu amene afunkhidwa ndi kuwalanda zinthu zawo,
23Kodi ndani wa inu amene adzamvetsera zimenezi
24Ndani anapereka Yakobo kwa ofunkha,
25Motero anawakwiyira kwambiri,