1Inu anthu a mitundu yonse, bwerani pafupi kuti mumve:
2Yehova wayipidwa ndi anthu a mitundu yonse;
3Anthu awo ophedwa adzatayidwa kunja,
4Dzuwa, mwezi ndi nyenyezi zidzasungunuka
5Yehova akuti, “Lupanga langa lakhutiratu magazi kumwamba;
6Lupanga la Yehova lakhuta magazi,
7Pamodzi ndi anthuwo zidzaphedwanso njati,
8Iyi ndi nthawi imene Yehova adzalipsira
9Madzi a mʼmitsinje ya Edomu adzasanduka phula,
10Motowo sudzazimitsidwa usiku ndi usana;
11Mʼdzikomo mudzakhala akabawi ndi anungu;
12Anthu olemekezeka ake sadzatchedwanso mfumu kumeneko;
13Minga idzamera mʼnyumba zake zankhondo zotetezedwa,
14Avumbwe adzakumana ndi afisi,
15Kadzidzi adzamangako chisa chake nʼkuyikirako mazira,
16Funafunani mʼbuku la Yehova ndi kuwerenga:
17Yehova wagawa dziko lawo;