We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 34

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 33 Yesaya Yesaya 35 →

1Inu anthu a mitundu yonse, bwerani pafupi kuti mumve:

2Yehova wayipidwa ndi anthu a mitundu yonse;

3Anthu awo ophedwa adzatayidwa kunja,

4Dzuwa, mwezi ndi nyenyezi zidzasungunuka

5Yehova akuti, “Lupanga langa lakhutiratu magazi kumwamba;

6Lupanga la Yehova lakhuta magazi,

7Pamodzi ndi anthuwo zidzaphedwanso njati,

8Iyi ndi nthawi imene Yehova adzalipsira

9Madzi a mʼmitsinje ya Edomu adzasanduka phula,

10Motowo sudzazimitsidwa usiku ndi usana;

11Mʼdzikomo mudzakhala akabawi ndi anungu;

12Anthu olemekezeka ake sadzatchedwanso mfumu kumeneko;

13Minga idzamera mʼnyumba zake zankhondo zotetezedwa,

14Avumbwe adzakumana ndi afisi,

15Kadzidzi adzamangako chisa chake nʼkuyikirako mazira,

16Funafunani mʼbuku la Yehova ndi kuwerenga:

17Yehova wagawa dziko lawo;

← Yesaya 33 Yesaya Yesaya 35 →