We Believe JesusFé, Esperança e Nova Vida

Yesaya 35

Biblica® Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero · nianja

← Yesaya 34 Yesaya Yesaya 36 →

1Chipululu ndi dziko lopanda madzi zidzasangalala;

2Dzikolo lidzakhala ndi maluwa ochuluka

3Limbitsani manja ofowoka,

4nenani kwa a mitima yamantha kuti;

5Pamenepo maso a anthu osaona adzapenyanso

6Anthu olumala adzalumpha ngati mbawala,

7mchenga wotentha udzasanduka dziwe,

8Ndipo kumeneko kudzakhala msewu waukulu;

9Kumeneko sikudzakhala mkango,

10Iwo amene Yehova anawawombola adzabwerera.

← Yesaya 34 Yesaya Yesaya 36 →