1Chipululu ndi dziko lopanda madzi zidzasangalala;
2Dzikolo lidzakhala ndi maluwa ochuluka
3Limbitsani manja ofowoka,
4nenani kwa a mitima yamantha kuti;
5Pamenepo maso a anthu osaona adzapenyanso
6Anthu olumala adzalumpha ngati mbawala,
7mchenga wotentha udzasanduka dziwe,
8Ndipo kumeneko kudzakhala msewu waukulu;
9Kumeneko sikudzakhala mkango,
10Iwo amene Yehova anawawombola adzabwerera.